Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 7:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Mwana wa Aroni amene wapereka kwa Mulungu magazi a nsembe zachiyanjano ndiponso mafuta, azitenga mwendo wakumbuyo wa kudzanja lamanja monga gawo lake.+

  • 1 Akorinto 9:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kodi simukudziwa kuti anthu ochita ntchito zopatulika amadya+ za m’kachisi, ndipo amene amatumikira+ kuguwa lansembe nthawi zonse amagawana gawo ndi guwa lansembe?

  • Levitiko 7:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 “‘Limeneli ndilo linali gawo la Aroni monga wansembe ndiponso gawo la ana ake monga ansembe. Gawoli linali lochokera pansembe zotentha ndi moto zoperekedwa kwa Yehova, malinga ndi zimene anawalamula pa tsiku limene anaperekedwa+ kuti atumikire monga ansembe a Yehova.

  • Deuteronomo 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “Ansembe achilevi, kapena kuti fuko lonse la Levi,+ asakhale ndi gawo kapena cholowa pakati pa Isiraeli. Iwo azidya nsembe zotentha ndi moto zoperekedwa kwa Yehova. Azidya cholowa chake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena