Numeri 18:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Yehova anapitiriza kulankhula ndi Aroni, kuti: “Iwe udzakhala wopanda cholowa m’dziko mwawo, ndipo sudzapatsidwa gawo lililonse pakati pawo.+ Ine ndine gawo lako ndi cholowa chako pakati pa ana a Isiraeli.+ Yoswa 13:33 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 33 Fuko la Alevi, Mose sanalipatse cholowa cha malo.+ Yehova Mulungu wa Isiraeli ndiye cholowa chawo, monga mmene anawalonjezera.+
20 Yehova anapitiriza kulankhula ndi Aroni, kuti: “Iwe udzakhala wopanda cholowa m’dziko mwawo, ndipo sudzapatsidwa gawo lililonse pakati pawo.+ Ine ndine gawo lako ndi cholowa chako pakati pa ana a Isiraeli.+
33 Fuko la Alevi, Mose sanalipatse cholowa cha malo.+ Yehova Mulungu wa Isiraeli ndiye cholowa chawo, monga mmene anawalonjezera.+