Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 18:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Popeza mwadzera njira yodutsa kwa kapolo wanu, mundilole ndikukonzereni kachakudya kuti mutsitsimutse mitima yanu.+ Mukatero mukhoza kupitiriza ulendo wanu.” Pamenepo iwo anati: “Chabwino, chita mmene waneneramo.”

  • Oweruza 19:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pa tsiku lachinayi, atadzuka m’mawa kwambiri monga mwa nthawi zonse, anakonzeka kuti anyamuke, koma bambo a mtsikanayo anauza mkamwini wawoyo kuti: “Yambani mwadya kaye mkate,+ kenako mukhoza kupita.”

  • Rute 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Boazi anadya ndi kumwa, ndipo anali wosangalala mumtima mwake.+ Kenako anapita kukagona chakumapeto kwa mulu wa balere. Ndiyeno Rute anayenda mwakachetechete ndi kuvundukula kumapazi kwa Boazi n’kugona.

  • Salimo 104:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Komanso kuti mutuluke vinyo amene amasangalatsa mtima wa munthu.+

      Amachita zonsezi kuti nkhope ya munthu isalale ndi mafuta,+

      Komanso kuti apereke chakudya chimene chimakhutiritsa mtima wa munthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena