Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 22:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Tsopano Mulungu anapsa mtima poona kuti Balamu akupita, moti mngelo wa Yehova anaima pamsewu kuti amutchingire njira.+ Balamuyo anali pabulu wake, ndipo anali ndi anyamata ake awiri.

  • Oweruza 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Zitatero, mwamuna wakeyo ananyamuka kukakambirana naye mofatsa kuti abwerere. Pa ulendowo anali limodzi ndi mtumiki wake+ ndi abulu awiri. Atafika kumeneko, mkaziyo analowetsa mwamuna wakeyo m’nyumba ya bambo ake ndipo iwo atamuona anasangalala kwambiri kukumana naye.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena