Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 20:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Tsopano amuna a Isiraeli anapita kukamenyana ndi ana a Benjamini ku Gibeya, ndipo kumeneko amuna a Isiraeliwo anafola mwa dongosolo lomenyera nkhondo.

  • Oweruza 20:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Koma anthuwo, amuna a Isiraeli, analimba mtima ndipo anapitanso kukafola mwa dongosolo lomenyera nkhondo pamalo omwe anafola tsiku loyamba lija.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena