Oweruza 5:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Mngelo wa Yehova+ anati: ‘Tembererani+ Merozi,Tembererani anthu ake mosaleka,Chifukwa sanathandize Yehova,Sanabwere ndi anthu amphamvu kudzathandiza Yehova.’ Oweruza 21:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Chotero khamu la Isiraelilo linatumiza amuna amphamvu kwambiri okwana 12,000, ndipo anawalamula kuti: “Pitani, mukaphe ndi lupanga anthu okhala ku Yabesi-giliyadi. Mukaphe ngakhale akazi ndi ana aang’ono.+
23 Mngelo wa Yehova+ anati: ‘Tembererani+ Merozi,Tembererani anthu ake mosaleka,Chifukwa sanathandize Yehova,Sanabwere ndi anthu amphamvu kudzathandiza Yehova.’
10 Chotero khamu la Isiraelilo linatumiza amuna amphamvu kwambiri okwana 12,000, ndipo anawalamula kuti: “Pitani, mukaphe ndi lupanga anthu okhala ku Yabesi-giliyadi. Mukaphe ngakhale akazi ndi ana aang’ono.+