Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 5:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mngelo wa Yehova+ anati: ‘Tembererani+ Merozi,

      Tembererani anthu ake mosaleka,

      Chifukwa sanathandize Yehova,

      Sanabwere ndi anthu amphamvu kudzathandiza Yehova.’

  • Oweruza 21:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chotero khamu la Isiraelilo linatumiza amuna amphamvu kwambiri okwana 12,000, ndipo anawalamula kuti: “Pitani, mukaphe ndi lupanga anthu okhala ku Yabesi-giliyadi. Mukaphe ngakhale akazi ndi ana aang’ono.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena