Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Anagawira cholowacho mafuko 9 ndi hafu, mwa kuchita maere,+ monga mmene Yehova analamulira kudzera mwa Mose.+

  • Oweruza 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Yoswa atauza anthuwo kuti apite, aliyense wa ana a Isiraeliwo anapita ku cholowa chake, kukatenga dzikolo kukhala lawo.+

  • Oweruza 20:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pamenepo anthu onse ananyamuka mogwirizana,+ ndipo anati: “Aliyense wa ife sapitanso ku hema wake kapena kupatukira kunyumba yake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena