Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pamenepo anthu onse ndi akulu amene anali pachipata anayankha kuti: “Ndife mboni! Yehova adalitse mkazi amene akulowa m’nyumba mwako kuti akhale ngati Rakele+ ndi Leya,+ akazi amene anabereka ana a nyumba ya Isiraeli.+ Uonetse kulemekezeka kwako mu Efurata+ ndi kudzipangira dzina m’Betelehemu.+

  • Rute 4:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Pamenepo akazi okhala naye pafupi+ anatcha mwanayo dzina lakuti Obedi.+ Ndipo iwo anati: “Mwana wabadwa kwa Naomi.” Obedi ndiye bambo ake a Jese,+ bambo ake a Davide.

  • Salimo 20:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Tidzafuula mokondwera chifukwa cha chipulumutso chanu,+

      Tidzakweza mbendera zathu m’dzina la Mulungu wathu.+

      Yehova akwaniritse zopempha zanu zonse.+

  • Mateyu 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Salimoni anabereka Boazi, ndipo mayi ake anali Rahabi.+

      Boazi anabereka Obedi, ndipo mayi ake anali Rute.+

      Obedi anabereka Jese.+

  • Mateyu 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yakobo anabereka Yosefe mwamuna wake wa Mariya, amene anabereka Yesu,+ wotchedwa Khristu.+

  • Aheberi 11:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndiponso, popanda chikhulupiriro+ n’zosatheka kukondweretsa Mulungu.+ Pakuti aliyense wofika kwa Mulungu ayenera kukhulupirira kuti iye alikodi,+ ndi kuti amapereka mphoto+ kwa anthu omufunafuna ndi mtima wonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena