Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 14:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Pamenepo Sauli anati: “Mulungu andilange mowirikiza+ ngati suufa ndithu,+ Yonatani.”

  • 1 Samueli 20:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Masiku onse amene mwana wa Jeseyo adzakhala ndi moyo, iweyo ndi ufumu wako sudzakhazikika ayi.+ Choncho tumiza anthu akamugwire ndi kumubweretsa kwa ine, pakuti ayenera kufa ndithu.”+

  • Miyambo 28:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Anthu okonda kuchita zoipa sangamvetse chilungamo, koma amene akufunafuna Yehova amamvetsa chilichonse.+

  • Miyambo 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mtsogoleri woipa wolamulira anthu onyozeka ali ngati mkango wobangula ndiponso chimbalangondo chimene chikubwera kudzakuluma.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena