Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mdaniyo anati, ‘Ndiwathamangira,+ ndi kuwapeza!+

      Ndigawa chuma chawo.+ Pamenepo moyo wanga ukhutira ndi zimene ndawachita!

      Ndisolola lupanga langa! Dzanja langa liwawononga!’+

  • 1 Samueli 23:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsopano Davide anayamba kukhala m’chipululu, m’malo ovuta kufikako. Iye anapitiriza kukhala m’dera lamapiri m’chipululu cha Zifi,+ ndipo Sauli anali kumufunafuna nthawi zonse,+ koma Mulungu sanam’pereke m’manja mwake.+

  • Salimo 71:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Iwo akunena kuti: “Mulungu wamusiya.+

      Mulondoleni ndi kumugwira pakuti palibe womulanditsa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena