Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yehova amandipatsa mphoto mogwirizana ndi chilungamo changa.+

      Amandibwezera mogwirizana ndi kuyera kwa manja anga.+

  • Salimo 91:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mulungu wanena kuti: “Popeza wasonyeza kuti amandikonda,+

      Inenso ndidzamupulumutsa.+

      Ndidzamuteteza chifukwa wadziwa dzina langa.+

  • Yohane 12:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ngati munthu wafuna kunditumikira ine, anditsatire, ndipo kumene ine ndidzakhala, mtumiki wanga adzakhalanso komweko.+ Aliyense wonditumikira ine, Atate adzamulemekeza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena