Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 “Yehova adzakutumizira matemberero,+ chisokonezo+ ndi chilango+ pa ntchito zako zonse zimene ukuyesa kugwira. Adzakuchitira zimenezi kufikira utafafanizidwa ndi kutha mofulumira, chifukwa cha kuipa kwa zochita zako popeza kuti wandisiya.+

  • 1 Samueli 28:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Sauli atamva zimenezi, anadzigwetsa mofulumira ndi kugona pansi mantha atamugwira kwambiri chifukwa cha mawu a “Samueli.” Komanso analefuka kwambiri chifukwa chakuti sanadye chakudya masana onse ndi usiku wonse.

  • Miyambo 10:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Chinthu choopsa kwa woipa n’chimene chidzamubwerere,+ koma anthu olungama adzapatsidwa zimene amalakalaka.+

  • Yesaya 57:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Oipa alibe mtendere,”+ akutero Mulungu wanga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena