-
Oweruza 21:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Ndiyeno akulu a khamulo ananena kuti: “Tsopano popeza kuti akazi awonongedwa m’fuko la Benjamini, tichita chiyani ndi amuna amene atsala opanda akaziwa?”
-