Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 28:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Ndiyeno uike Urimu+ ndi Tumimu m’chovala pachifuwa chachiweruzo, ndipo zizikhala pamtima pa Aroni akamalowa kukaonekera pamaso pa Yehova. Aroni azinyamula ziweruzo+ za ana a Isiraeli pamtima pake poonekera kwa Yehova nthawi zonse.

  • Levitiko 8:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Anamuveka chovala cha pachifuwa+ ndi kuika Urimu ndi Tumimu+ m’chovala cha pachifuwacho.

  • Deuteronomo 33:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndipo kwa Levi anati:+

      “Tumimu ndi Urimu+ wanu ndizo za munthu wokhulupirika kwa inu,+

      Amene munamuyesa pa Masa.+

      Munayamba kulimbana naye pafupi ndi madzi a Meriba.+

  • Ezara 2:63
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 63 Pa chifukwa chimenechi, Tirisata*+ anawauza kuti sayenera kudya+ zinthu zopatulika koposa, kufikira patakhala wansembe wokhala ndi Urimu+ ndi Tumimu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena