Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mwamunayo anayankha kuti: “Mkazi amene munandipatsayu ndi amene wandipatsa chipatso cha mtengowo, ndipo ine ndadya.”+

  • Ekisodo 32:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndipo Aroni anayankha kuti: “Mkwiyo wa mbuyanga usayake. Inuyo mukuwadziwa bwino anthuwa, kuti amakonda kuchita zoipa.+

  • 1 Samueli 15:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Anthuwa+ atenga pa zofunkha, nkhosa ndi ng’ombe zabwino kwambiri, pa zinthu zimene zinayenera kuwonongedwa, kuti azipereke nsembe+ kwa Yehova Mulungu wanu ku Giligala.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena