Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 17:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Pamenepo Davide anapisa dzanja m’chikwama chake ndi kutengamo mwala. Kenako anauponya ndi gulaye moti unamenya+ Mfilisiti uja pamphumi n’kuloweratu m’mutu mwake, ndipo anagwa pansi chafufumimba.+

  • Salimo 18:39
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Inu mudzandiveka mphamvu kuti ndithe kumenya nkhondo.

      Mudzakomola ondiukira.+

  • Salimo 44:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndi thandizo lanu tidzakankha adani athu.+

      M’dzina lanu tidzapondereza amene akutiukira.+

  • Salimo 144:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iye amandisonyeza kukoma mtima kwake kosatha ndipo ndiye malo anga achitetezo,+

      Malo anga okwezeka ndi Wopereka chipulumutso,+

      Chishango+ changa ndi malo anga othawirako.+

      Iye amandigonjetsera mitundu ya anthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena