Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 14:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndalamazo udzagulire chilichonse chimene mtima wako wakhumba,+ kaya ndi ng’ombe, nkhosa, mbuzi, vinyo, chakumwa choledzeretsa+ ndi chilichonse chimene mtima wako wafuna. Ndipo uzidzadya zinthuzi pamaso pa Yehova Mulungu wako ndi kukondwera,+ iweyo ndi banja lako.

  • 1 Mafumu 11:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Ndidzasankha iweyo, ndipo udzalamuliradi zonse zimene moyo wako umakhumba.+ Udzakhaladi mfumu ya Isiraeli.

  • Salimo 20:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Akupatseni zokhumba za mtima wanu,+

      Ndipo akwaniritse zofuna zanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena