Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 14:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Mkazi wa Sauli dzina lake anali Ahinowamu, mwana wamkazi wa Ahimazi. Mkulu wa gulu lake lankhondo anali Abineri+ mwana wa Nera, m’bale wa bambo ake a Sauli.

  • 2 Samueli 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ndiyeno Abineri+ mwana wa Nera, amene anali mtsogoleri wa asilikali a Sauli, anatenga Isi-boseti+ mwana wa Sauli ndi kuwolokera naye ku Mahanaimu.+

  • 2 Samueli 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Chotero, Abineri anatumiza mithenga kwa Davide nthawi yomweyo, kuti akamuuze kuti: “Kodi mwini dziko ndani?” Ndiyeno anawonjezera kuti: “Chita nane pangano, ndipo inetu ndidzakuthandiza kutembenuza Isiraeli yense kukhala kumbali yako.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena