Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 20:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ndiyeno anauza mtumiki wakeyo kuti: “Chonde, thamanga kuti ukatole mivi imene ndikuponya.”+ Mtumikiyo anathamanga, ndipo Yonatani anaponya muvi kuti upitirire mtumikiyo.

  • 1 Samueli 31:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Nkhondo inam’kulira kwambiri Sauli, moti pamapeto pake oponya mivi ndi uta anamupeza ndipo anamuvulaza koopsa.+

  • 2 Samueli 1:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Uta wa Yonatani sunkalephera kupha adani ndi kukhetsa magazi awo,

      Sunkalephera kubaya mafuta a anthu amphamvu.+

      Lupanga la Sauli silinkabwerako chabe osakwaniritsa ntchito yake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena