Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 47:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pakuti Mulungu ndi Mfumu ya dziko lonse lapansi.+

      Imbani nyimbo zotamanda ndi kuchita zinthu mozindikira.+

  • Salimo 83:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kuti anthu adziwe+ kuti inu, amene dzina lanu ndinu Yehova,+

      Inu nokha ndinu Wam’mwambamwamba,+ wolamulira dziko lonse lapansi.+

  • Salimo 97:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti inu Yehova, ndinu Wam’mwambamwamba wolamulira dziko lonse lapansi.+

      Mwakwera pamwamba kwambiri kuposa milungu ina yonse.+

  • Salimo 115:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Musalole kuti mitundu izinena kuti:+

      “Mulungu wawo ali kuti tsopano?”+

  • Aroma 1:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Chifukwa chakuti, ngakhale anam’dziwa Mulungu, iwo sanam’patse ulemerero monga Mulungu kapena kumuyamikira.+ M’malomwake anayamba kulingalira zinthu zopanda pake+ ndipo mtima wawo wopusawo unachita mdima.+

  • 1 Akorinto 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno pa nkhani ya kudya+ zakudya zoperekedwa kwa mafano, timadziwa kuti fano ndi lopanda pake+ m’dziko, ndiponso kuti kulibe Mulungu wina koma mmodzi yekha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena