-
2 Samueli 13:10Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
10 Ndiyeno Aminoni anauza Tamara kuti: “Bweretsa chakudya chonditonthoza kuchipinda chogona kuti ndidye kuchokera m’manja mwako monga wodwala.” Pamenepo Tamara anatenga makeke amene anapangawo ndi kupita nawo kwa Aminoni m’bale wake m’chipinda chogona.
-