Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 5:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Tsopano wansembeyo azilumbiritsa mkaziyo ndi lumbiro la temberero.+ Iye aziti kwa mkaziyo: “Yehova akuike kukhala chitsanzo cha temberero ndi lumbiroli pakati pa anthu amtundu wako. Yehova achite zimenezo mwa kufotetsa ntchafu*+ yako, ndi kutupitsa mimba yako.

  • Deuteronomo 29:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yehova sadzafuna kukhululukira+ munthu woteroyo, m’malomwake mkwiyo+ ndi ukali+ wa Yehova udzamuyakira,+ ndipo matemberero onse olembedwa m’buku+ ili adzakhala pa iye, motero Yehova adzafafanizadi dzina la munthuyo pansi pa thambo.

  • 2 Mbiri 34:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 “Yehova wanena kuti, ‘Ndibweretsa tsoka+ pamalo ano ndi anthu ake,+ pokwaniritsa matemberero onse+ amene analembedwa m’buku limene anawerenga pamaso pa mfumu ya Yuda,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena