Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 86:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu Yehova, ndilangizeni za njira yanu.+

      Ndidzayenda m’choonadi chanu.+

      Ndipatseni mtima wosagawanika kuti ndiope dzina lanu.+

  • Salimo 119:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  36 Ndithandizeni kuti mtima wanga uziganizira zikumbutso zanu,+

      Osati kupeza phindu.*+

  • 2 Atesalonika 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ambuye apitirize kutsogolera mitima yanu kuti muzikonda+ Mulungu ndi kuti muzipirira+ chifukwa cha Khristu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena