Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 22:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako Hilikiya+ mkulu wa ansembe anauza Safani+ mlembi+ kuti: “Ndapeza buku la chilamulo+ m’nyumba ya Yehova!” Choncho Hilikiya anapereka bukulo kwa Safani, ndipo iye anayamba kuliwerenga.

  • 2 Mbiri 34:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Itatero, mfumuyo inapita kunyumba ya Yehova+ limodzi ndi amuna onse a ku Yuda, anthu okhala ku Yerusalemu, ansembe,+ Alevi, ndi anthu onse, wamng’ono ndi wamkulu yemwe. Tsopano mfumuyo inayamba kuwawerengera+ mawu onse a m’buku la pangano limene linapezeka panyumba ya Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena