Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 18:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Tsopano Davide anali atakhala pakati pa zipata ziwiri.+ Pa nthawiyi mlonda+ anakwera padenga la mpanda kuchipata. Ndiyeno atakweza maso anaona munthu akuthamanga ali yekha.

  • 2 Samueli 18:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Kenako mlonda uja anaonanso munthu wina akuthamanga. Ndiyeno mlondayo anaitana mlonda wa pachipata ndi kumuuza kuti: “Taona! Munthu winanso akuthamanga ali yekha.” Pamenepo mfumu inati: “Ameneyunso akubweretsa uthenga.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena