1 Mbiri 23:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Kenako anasonkhanitsa akalonga onse+ a Isiraeli komanso ansembe+ ndi Alevi.+ 1 Mbiri 26:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Kumbali ya Alevi, Ahiya anali kuyang’anira chuma+ cha m’nyumba ya Mulungu woona, ndi chuma cha zinthu zimene anaziyeretsa kukhala zopatulika.+
20 Kumbali ya Alevi, Ahiya anali kuyang’anira chuma+ cha m’nyumba ya Mulungu woona, ndi chuma cha zinthu zimene anaziyeretsa kukhala zopatulika.+