Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno wansembeyo aone nthenda imene yatuluka pakhunguyo.+ Ngati cheya cha pamalopo chasanduka choyera ndipo pakuoneka kuti m’pozama kupitirira khungu, ndiye kuti limenelo ndi khate. Wansembe aone nthendayo n’kugamula kuti munthuyo ndi wodetsedwa.

  • Deuteronomo 24:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Samalani ndi mliri wa khate+ ndi kuonetsetsa kuti mukuchita zonse zimene ansembe achilevi adzakulangizani.+ Muzichita mosamala zonse zimene ndawalamula.+

  • Miyambo 11:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Kodi kudzikweza kwafika? Ndiye kuti manyazinso afika.+ Koma nzeru zimakhala ndi anthu odzichepetsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena