Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Munthu akatuluka zotupa, kapena nkhanambo,+ kapena chikanga pakhungu lake, ndipo chasintha n’kukhala nthenda ya khate,+ azibwera naye kwa Aroni wansembe, kapena kwa mmodzi wa ana ake amenenso ndi ansembe.+

  • Levitiko 13:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Wansembe+ aziona zilondazo ndi kugamula kuti munthuyo ndi wodetsedwa chifukwa cha zilondazo. Limenelo ndi khate.+

  • 2 Mbiri 26:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Wansembe wamkulu Azariya ndi ansembe ena onse atamuyang’ana, anangoona kuti wachita khate pamphumi.+ Choncho anayamba kumutulutsa msangamsanga, ndipo mwiniwakeyonso anatuluka mofulumira chifukwa Yehova anali atamulanga.+

  • Malaki 2:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Wansembe ayenera kuphunzitsa anthu kuti adziwe Mulungu. Anthuwo ayenera kufunafuna kumva chilamulo kuchokera pakamwa pake,+ pakuti iye ndi mthenga wa Yehova wa makamu.+

  • Maliko 1:44
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 44 Anamuuza kuti: “Samala, usauze aliyense zimenezi, koma upite ukadzionetse kwa wansembe+ ndipo ukapereke zinthu zimene Mose analamula+ chifukwa cha kuyeretsedwa kwako, kuti zikhale umboni kwa iwo.”+

  • Luka 17:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Yesu atawaona anawauza kuti: “Pitani mukadzionetse kwa ansembe.”+ Ndiyeno pamene anali kupita anayeretsedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena