Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno patapita nthawi, ana a Amoni anayamba kumenyana ndi Aisiraeli.+

  • 2 Samueli 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pambuyo pake, mfumu ya ana a Amoni+ inamwalira, ndipo Hanuni mwana wake anayamba kulamulira m’malo mwa bambo ake.+

  • 2 Mbiri 20:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Pambuyo pake ana a Mowabu,+ ana a Amoni,+ pamodzi ndi Aamonimu+ ena, anabwera kudzamenyana ndi Yehosafati.+

  • Yeremiya 49:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Ponena za ana a Amoni+ Yehova wanena kuti: “Kodi Isiraeli alibe ana aamuna, kapena kodi alibe wolandira cholowa? N’chifukwa chiyani Malikamu+ watenga Gadi+ kukhala cholowa chake? N’chifukwa chiyani anthu olambira Malikamu akukhala m’mizinda ya Isiraeli?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena