Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 17:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Mitundu imeneyi inali kuopa Yehova,+ koma inali kutumikira zifaniziro zawo zogoba. Mpaka lero, ana awo ndi zidzukulu zawo akuchitabe mmene makolo awo ankachitira.

  • 2 Mbiri 33:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Nkhani zokhudza pemphero lake,+ zokhudza mmene Mulungu anamvera kupembedza kwake,+ machimo ake onse,+ ndi kusakhulupirika kwake+ zinalembedwa m’mawu a amasomphenya ake. M’mawu amenewa munalembedwanso nkhani zokhudza malo amene iye anamangako malo okwezeka+ n’kuikapo mizati yopatulika+ ndi zifaniziro zogoba+ asanadzichepetse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena