Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 16:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Kodi amuna inu mukuyesa n’chinthu chaching’ono kuti Mulungu wa Isiraeli anakupatulani+ pakati pa Aisiraeli, n’kukutengani kukhala akeake, kuti muzitumikira Yehova pachihema chake ndi kutumikira khamulo?+

  • Salimo 2:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tumikirani Yehova mwamantha.+

      Kondwerani ndipo nthunthumirani.+

  • Salimo 100:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Tumikirani Yehova mokondwera.+

      Bwerani kwa iye mukufuula mosangalala.+

  • Tito 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Ine Paulo, kapolo+ wa Mulungu ndi mtumwi+ wa Yesu Khristu, ndili ndi chikhulupiriro chogwirizana ndi cha anthu osankhidwa+ ndi Mulungu. Komanso ndine wodziwa molondola+ choonadi+ chokhudza kudzipereka kwathu kwa Mulungu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena