Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Choncho Mose ndi Aroni anapita kwa Farao ndi kumuuza kuti: “Yehova Mulungu wa Aheberi wanena kuti, ‘Udzakana kundigonjera kufikira liti?+ Lola anthu anga apite kuti akanditumikire.

  • 2 Mbiri 32:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Komabe, Hezekiya anadzichepetsa+ pambuyo pa kudzikuza kwa mtima wake. Anadzichepetsa limodzi ndi anthu a ku Yerusalemu, ndipo mkwiyo wa Yehova sunawagwere m’masiku a Hezekiya.+

  • Danieli 5:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 “Koma inuyo a Belisazara,+ amene ndinu mwana wake, simunadzichepetse mumtima mwanu+ ngakhale kuti munali kudziwa zonsezi.+

  • Yakobo 4:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Dzichepetseni pamaso pa Yehova,+ ndipo iye adzakukwezani.+

  • 1 Petulo 5:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Choncho dzichepetseni pansi pa dzanja lamphamvu la Mulungu, kuti adzakukwezeni m’nthawi yake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena