Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 52:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Lilime lako limakonza chiwembu, ndipo ndi lakuthwa ngati lezala,+

      Limachita zachinyengo.+

  • Salimo 119:69
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  69 Anthu odzikuza andinenera mabodza ambiri,+

      Koma ine ndidzasunga malamulo anu ndi mtima wanga wonse.+

  • Chivumbulutso 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndipo ndinamva mawu ofuula kumwamba, akuti:

      “Tsopano chipulumutso,+ mphamvu,+ ufumu wa Mulungu wathu,+ ndi ulamuliro wa Khristu+ wake zafika, chifukwa woneneza abale athu waponyedwa pansi. Iyeyo anali kuwaneneza usana ndi usiku pamaso pa Mulungu wathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena