Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chivumbulutso 12
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

Chivumbulutso 12:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Chv 1:1
  • +Yes 54:1, 5; Aga 4:26

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 177-178

    Kukhala ndi Moyo Kosatha, tsa. 117

Chivumbulutso 12:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 3:16

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 177-178

Chivumbulutso 12:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Chv 12:9; 20:2

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mapeto a Chivumbulutso, tsa. 178

    Nsanja ya Olonda,

    9/1/2001, tsa. 6

    4/1/1989, tsa. 20

Chivumbulutso 12:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 9:15
  • +Ge 6:2; Yob 38:7; 2Ak 11:15
  • +2Pe 2:4; Yuda 6
  • +Ge 3:15
  • +Yes 66:9
  • +Yer 51:34

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    5/2018, tsa. 23

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 178-179

Chivumbulutso 12:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Chv 11:15
  • +Sl 2:9; 110:2; Chv 19:15
  • +Sl 2:6; 110:1

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 177, 179-180

    Kukhala ndi Moyo Kosatha, tsa. 117

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/1988, tsa. 14

Chivumbulutso 12:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 55:7
  • +1Mf 19:6; Miy 30:8
  • +Chv 11:3; 12:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 32

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 179-180, 184

Chivumbulutso 12:7

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Da 10:13; 12:1; Yuda 9

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo,

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 24

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 180-182

    Nsanja ya Olonda,

    7/1/1990, tsa. 26

    Mawu a Mulungu, ptsa. 159-160

Chivumbulutso 12:8

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 24

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 180-182

Chivumbulutso 12:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Chv 12:3; 20:2
  • +Ge 3:1; 2Ak 11:3; Chv 12:14
  • +Mt 4:1; Yoh 8:44; Ahe 2:14; Yak 4:7; 1Pe 5:8
  • +1Mb 21:1; Yob 1:6; Zek 3:2; Mt 4:10; Yoh 13:27; Aro 16:20; 2At 2:9
  • +2Ak 4:4; 11:14; Aef 2:2; 1Yo 5:19
  • +Lu 10:18; Chv 12:13

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 24

    Nsanja ya Olonda,

    5/15/2015, ptsa. 9-10

    5/15/2009, tsa. 18

    2/15/2004, tsa. 16

    Galamukani!,

    8/2010, ptsa. 20-21

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 180-182

    Mawu a Mulungu, ptsa. 159-160

Chivumbulutso 12:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 118:14; Lu 1:69; Aro 13:11; 2Ak 6:2; Ahe 9:28; 1Pe 1:5
  • +Chv 11:17
  • +Chv 11:15
  • +Mt 24:30; 25:32; 2Ak 5:10; Aef 1:10; 1At 4:16
  • +Yob 1:9; Zek 3:1

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Zimene Baibulo Limaphunzitsa, tsa. 86

    Baibulo Limaphunzitsa Chiyani, ptsa. 79-80

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2006, tsa. 22

    4/15/1999, tsa. 17

    12/15/1990, ptsa. 19-20

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 182-183

    Chisungiko cha Padziko Lonse, ptsa. 91-92

Chivumbulutso 12:11

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Yo 2:14
  • +1Pe 1:19
  • +Mac 1:8; 2Ti 1:8; Chv 1:9; 19:10
  • +Mt 16:25; Lu 14:26; Mac 20:24

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    7/1/2007, tsa. 31

    12/15/1990, ptsa. 19-20

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 182-183

Chivumbulutso 12:12

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 7:53; Ahe 12:22; Chv 13:6
  • +Chv 8:13
  • +Yes 57:20; 60:2; Chv 17:15
  • +Da 8:19; Mik 4:1; Mt 24:34; Aro 16:20; 2Ti 3:1; 2Pe 3:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 24

    Zimene Baibulo Limaphunzitsa, ptsa. 86-87

    Baibulo Limaphunzitsa Chiyani, tsa. 80

    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira, tsa. 22

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 182-183

    Nsanja ya Olonda,

    10/15/2001, tsa. 6

    10/1/1999, tsa. 4

    4/1/1996, tsa. 18

    11/1/1995, tsa. 19

    12/15/1988, tsa. 14

    Mawu a Mulungu, ptsa. 160-161

    Kukhala ndi Moyo Kosatha, tsa. 137

Chivumbulutso 12:13

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Lu 10:18
  • +Ge 3:15; Chv 12:1

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 183-184

Chivumbulutso 12:14

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Eks 19:4; Yes 40:31
  • +Sl 55:7
  • +Mt 4:4; Lu 12:42
  • +Chv 11:3; 12:6
  • +Ge 3:1; 2Ak 11:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, lesson 32

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 183-184

Chivumbulutso 12:15

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Sl 18:4; Yes 17:12
  • +Da 11:40

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    5/2020, tsa. 6

    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira, ptsa. 150-151

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 184-185

    Nsanja ya Olonda,

    12/15/1988, tsa. 14

Chivumbulutso 12:16

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Tit 3:1; Chv 13:11

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    5/2022, tsa. 6

    Kuchitira Umboni Mokwanira, tsa. 164

    Utumiki Komanso Moyo Wathu,

    12/2019, tsa. 8

    Ufumu wa Mulungu Ukulamulira, tsa. 151

    Nsanja ya Olonda,

    1/15/2009, tsa. 32

    11/1/1990, tsa. 15

    12/15/1988, tsa. 14

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 185-186

Chivumbulutso 12:17

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ge 3:15
  • +Mt 24:9; Mac 1:8; Chv 1:9; 6:9

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda (Yophunzira),

    5/2022, ptsa. 5-6, 16

    Mapeto a Chivumbulutso, ptsa. 11-12, 183, 185-186, 279

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

Chiv. 12:1Chv 1:1
Chiv. 12:1Yes 54:1, 5; Aga 4:26
Chiv. 12:2Ge 3:16
Chiv. 12:3Chv 12:9; 20:2
Chiv. 12:4Yes 9:15
Chiv. 12:4Ge 6:2; Yob 38:7; 2Ak 11:15
Chiv. 12:42Pe 2:4; Yuda 6
Chiv. 12:4Ge 3:15
Chiv. 12:4Yes 66:9
Chiv. 12:4Yer 51:34
Chiv. 12:5Chv 11:15
Chiv. 12:5Sl 2:9; 110:2; Chv 19:15
Chiv. 12:5Sl 2:6; 110:1
Chiv. 12:6Sl 55:7
Chiv. 12:61Mf 19:6; Miy 30:8
Chiv. 12:6Chv 11:3; 12:14
Chiv. 12:7Da 10:13; 12:1; Yuda 9
Chiv. 12:9Chv 12:3; 20:2
Chiv. 12:9Ge 3:1; 2Ak 11:3; Chv 12:14
Chiv. 12:9Mt 4:1; Yoh 8:44; Ahe 2:14; Yak 4:7; 1Pe 5:8
Chiv. 12:91Mb 21:1; Yob 1:6; Zek 3:2; Mt 4:10; Yoh 13:27; Aro 16:20; 2At 2:9
Chiv. 12:92Ak 4:4; 11:14; Aef 2:2; 1Yo 5:19
Chiv. 12:9Lu 10:18; Chv 12:13
Chiv. 12:10Sl 118:14; Lu 1:69; Aro 13:11; 2Ak 6:2; Ahe 9:28; 1Pe 1:5
Chiv. 12:10Chv 11:17
Chiv. 12:10Chv 11:15
Chiv. 12:10Mt 24:30; 25:32; 2Ak 5:10; Aef 1:10; 1At 4:16
Chiv. 12:10Yob 1:9; Zek 3:1
Chiv. 12:111Yo 2:14
Chiv. 12:111Pe 1:19
Chiv. 12:11Mac 1:8; 2Ti 1:8; Chv 1:9; 19:10
Chiv. 12:11Mt 16:25; Lu 14:26; Mac 20:24
Chiv. 12:12Mac 7:53; Ahe 12:22; Chv 13:6
Chiv. 12:12Chv 8:13
Chiv. 12:12Yes 57:20; 60:2; Chv 17:15
Chiv. 12:12Da 8:19; Mik 4:1; Mt 24:34; Aro 16:20; 2Ti 3:1; 2Pe 3:3
Chiv. 12:13Lu 10:18
Chiv. 12:13Ge 3:15; Chv 12:1
Chiv. 12:14Eks 19:4; Yes 40:31
Chiv. 12:14Sl 55:7
Chiv. 12:14Mt 4:4; Lu 12:42
Chiv. 12:14Chv 11:3; 12:6
Chiv. 12:14Ge 3:1; 2Ak 11:3
Chiv. 12:15Sl 18:4; Yes 17:12
Chiv. 12:15Da 11:40
Chiv. 12:16Tit 3:1; Chv 13:11
Chiv. 12:17Ge 3:15
Chiv. 12:17Mt 24:9; Mac 1:8; Chv 1:9; 6:9
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
  • 11
  • 12
  • 13
  • 14
  • 15
  • 16
  • 17
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
Chivumbulutso 12:1-17

Chivumbulutso

12 Kenako chizindikiro chachikulu+ chinaoneka kumwamba. Ndicho mkazi+ atavala dzuwa, ndipo mwezi unali kunsi kwa mapazi ake. Kumutu kwake kunali chisoti chachifumu chokhala ndi nyenyezi 12, 2 ndipo mkaziyo anali ndi pakati. Iye analira pomva ululu+ chifukwa cha zowawa za pobereka.

3 Chizindikiro chinanso chinaoneka kumwamba, ndipo ndinaona chinjoka chachikulu+ chofiira, chokhala ndi mitu 7 ndi nyanga 10, ndipo pamitupo panali zisoti zachifumu 7. 4 Mchira+ wake unakokolola gawo limodzi mwa magawo atatu a nyenyezi+ zakumwamba n’kuzigwetsera kudziko lapansi.+ Ndipo chinjokacho chinangoimabe pamaso pa mkazi uja,+ amene anali pafupi kubereka,+ kuti akabereka chidye+ mwana wakeyo.

5 Mkaziyo anabereka mwana wamwamuna,+ mnyamata amene adzakusa mitundu yonse ndi ndodo yachitsulo.+ Ndipo mwana wakeyo anatengedwa msangamsanga n’kupititsidwa kwa Mulungu ndi kumpando wake wachifumu.+ 6 Koma mkaziyo anathawira kuchipululu,+ kumene Mulungu anamukonzera malo, kuti akadyetsedwe+ masiku 1,260.+

7 Ndipo kumwamba kunabuka nkhondo: Mikayeli+ ndi angelo ake anamenyana ndi chinjoka. Chinjokacho ndi angelo ake chinamenya nkhondo, 8 koma sichinapambane, ndipo malo awo sanapezekenso kumwamba. 9 Choncho chinjokacho+ chinaponyedwa pansi, njoka yakale ija,+ iye wotchedwa Mdyerekezi+ ndi Satana,+ amene akusocheretsa dziko lonse lapansi+ kumene kuli anthu. Iye anaponyedwa kudziko lapansi,+ ndipo angelo akenso anaponyedwa naye limodzi. 10 Ndipo ndinamva mawu ofuula kumwamba, akuti:

“Tsopano chipulumutso,+ mphamvu,+ ufumu wa Mulungu wathu,+ ndi ulamuliro wa Khristu+ wake zafika, chifukwa woneneza abale athu waponyedwa pansi. Iyeyo anali kuwaneneza usana ndi usiku pamaso pa Mulungu wathu.+ 11 Iwo anamugonjetsa+ chifukwa cha magazi a Mwanawankhosa,+ ndiponso chifukwa cha mawu a umboni wawo.+ Ndipo iwo sanaone kuti miyoyo yawo ndi yofunika,+ ngakhale pamene anali pa ngozi yoti akhoza kufa. 12 Pa chifukwa chimenechi, kondwerani kumwamba inu ndi inu okhala kumeneko!+ Tsoka+ dziko lapansi ndi nyanja,+ chifukwa Mdyerekezi watsikira kwa inu, ndipo ali ndi mkwiyo waukulu podziwa kuti wangotsala ndi kanthawi kochepa.”+

13 Tsopano chinjoka chitaona kuti achigwetsera kudziko lapansi,+ chinazunza mkazi+ amene anabereka mwana wamwamuna uja. 14 Koma mkaziyo anapatsidwa mapiko awiri+ a chiwombankhanga chachikulu kuti aulukire kuchipululu,+ kumalo ake aja. Kumeneko n’kumene akudyetsedwa+ kwa nthawi imodzi, nthawi ziwiri, ndi hafu ya nthawi,+ kutali ndi njoka ija.+

15 Kenako njokayo inalavula madzi+ ngati mtsinje kuchokera m’kamwa mwake, kulavulira mkazi uja, kuti amizidwe ndi mtsinjewo.+ 16 Koma dziko lapansi linathandiza mkaziyo.+ Dzikolo linatsegula pakamwa pake ndi kumeza mtsinje umene chinjoka chija chinalavula kuchokera m’kamwa mwake. 17 Ndipo chinjokacho chinakwiya ndi mkazi uja,+ moti chinapita kukachita nkhondo ndi otsala a mbewu yake, amene amasunga malamulo a Mulungu, amenenso ali ndi ntchito yochitira umboni+ za Yesu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena