Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano anthu amene anali kugwira ntchito yomanga nyumbayo anamaliza kumanga maziko+ a kachisi wa Yehova. Atatero, ansembe ovala zovala zaunsembe+ omwe ananyamula malipenga,+ ndiponso Alevi ana a Asafu+ omwe ananyamula zinganga,+ anaimirira kuti atamande Yehova motsatira dongosolo+ limene Davide mfumu ya Isiraeli anakhazikitsa.

  • Hagai 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “‘Ganizirani mofatsa+ zimene zichitike kuyambira lero mpaka m’tsogolo. Muganizire mofatsa zimene zinachitika kuyambira pa tsiku la 24 la mwezi wa 9, pamene maziko a kachisi wa Yehova anayalidwa.+ Ganizirani izi mofatsa:

  • Zekariya 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Manja a Zerubabele anayala maziko a nyumbayi,+ ndipo manja ake omwewo adzaimalizitsa.+ Pamenepo mudzadziwa kuti Yehova wa makamu wandituma kwa inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena