Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pa ana a Pahati-mowabu+ panali Eliho-enai mwana wa Zerahiya. Iye anali ndi amuna 200.

  • Ezara 10:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Pa ana a Pahati-mowabu+ panali Adena, Kelali, Benaya, Maaseya, Mataniya, Bezaleli, Binui ndi Manase.

  • Nehemiya 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Malikiya mwana wamwamuna wa Harimu,+ komanso Hasubu mwana wamwamuna wa Pahati-mowabu,+ anakonza gawo lina la mpandawo, ndipo anakonzanso Nsanja ya Mauvuni.+

  • Nehemiya 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ana a Pahati-mowabu,+ ochokera mwa ana a Yesuwa ndi Yowabu,+ 2,818.

  • Nehemiya 10:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Atsogoleri awa a anthu anatsimikiziranso panganoli: Parosi, Pahati-mowabu,+ Elamu, Zatu, Bani,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena