Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoweli 3:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mitunduyi inali kuchitira maere anthu anga+ ndipo inali kupereka mwana wamwamuna kuti akhale malipiro a hule.+ Inali kupereka mwana wamkazi kuti akhale malipiro a vinyo woti amwe.

  • Obadiya 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pa tsiku limene unangoima n’kumaonerera, pa tsiku limene alendo anagwira gulu la asilikali la m’bale wako n’kupita nalo kudziko lina,+ ndiponso pamene alendo enieni analowa pazipata za mzinda wake+ n’kuchita maere pa Yerusalemu,+ iwe unali ngati mmodzi wa adani akewo.

  • Mateyu 27:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Atam’pachika+ anagawana malaya ake akunja+ mwa kuchita maere,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena