Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 22:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji ine?+

      N’chifukwa chiyani mukuchedwa kundipulumutsa?+

      N’chifukwa chiyani simukumva mawu a kubuula kwanga?+

  • Salimo 38:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndalefuka ndipo ndaponderezeka kwambiri.

      Ndikulira mofuula chifukwa cha kuvutika kwa mtima wanga.+

  • Yesaya 59:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Tonsefe tikungolira ngati zimbalangondo ndipo tikungokhalira kubuula momvetsa chisoni ngati njiwa.+ Tinali kuyembekezera chilungamo+ koma sichinabwere. Tinali kuyembekezera chipulumutso koma chakhala nafe kutali.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena