Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 104:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mkango wamphamvu umabangula pofunafuna nyama,+

      Ndiponso popempha chakudya kwa Mulungu.+

  • Salimo 145:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Zolengedwa zonse zimayang’ana kwa inu mwachiyembekezo,+

      Ndipo mumazipatsa chakudya pa nyengo yake.+

  • Nahumu 2:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mkango unali kukhadzulakhadzula nyama yokwanira kuti udyetse ana ake ndipo unali kupha nyama kuti upatse mikango yaikazi. Mapanga ake anali kukhala odzaza ndi nyama, ndipo malo ake obisalamo anali ndi nyama zokhadzulakhadzula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena