Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwo ayasamula kukamwa kwawo kuti andimeze.+

      Andimenya mbama ndi mnyozo.

      Asonkhana ambirimbiri kuti alimbane nane.+

  • Yobu 16:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anzanga asanduka ondilankhulira otsutsana nane.+

      Diso langa lakhala likuyang’ana kwa Mulungu osagona.+

  • Yobu 17:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndithu, onyoza andizungulira,+

      Ndipo diso langa likuyang’anitsitsa khalidwe lawo lopanduka.

  • Aheberi 11:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ena analandira mayesero awo mwa kutonzedwa ndi kukwapulidwa, komanso kuposa pamenepo, mwa maunyolo+ ndi ndende.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena