Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 31:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye adzandiyeza pasikelo zolondola,+

      Ndipo Mulungu adzadziwa kuti ndili ndi mtima wosagawanika.+

  • Salimo 17:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Mwasanthula mtima wanga, mwandifufuza usiku,+

      Ndipo mwandiyenga. Mudzaona kuti sindinaganizire kuchita choipa chilichonse.+

      Pakamwa panga sipadzaphwanya malamulo.+

  • 1 Petulo 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Zimenezi zikukuchitikirani kuti chikhulupiriro chanu, chimene chayesedwa+ ndipo n’chamtengo wapatali kuposa golide amene amawonongekabe ngakhale kuti anadutsa m’moto,+ chidzakuchititseni kutamandidwa ndiponso kulandira ulemerero ndi ulemu, zochita za Yesu Khristu zikadzaululika.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena