Deuteronomo 32:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Iye ndi Thanthwe, ndipo ntchito yake ndi yangwiro,+Njira zake zonse ndi zolungama.+Mulungu wokhulupirika,+ amene sachita chosalungama.+Iye ndi wolungama ndi wowongoka.+ Deuteronomo 32:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Anapitiriza kumuyendetsa pamapiri a dziko lapansi,+Moti anadya zokolola za m’minda.+Anapitirizanso kumudyetsa uchi wochokera m’thanthwe,+Ndi mafuta ochokera m’mwala wa nsangalabwi.+ Deuteronomo 33:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Kwa Aseri anati:+“Aseri ndi wodalitsidwa ndi ana aamuna.+Akhale wovomerezeka ndi abale ake,+Woponda phazi lake m’mafuta.+
4 Iye ndi Thanthwe, ndipo ntchito yake ndi yangwiro,+Njira zake zonse ndi zolungama.+Mulungu wokhulupirika,+ amene sachita chosalungama.+Iye ndi wolungama ndi wowongoka.+
13 Anapitiriza kumuyendetsa pamapiri a dziko lapansi,+Moti anadya zokolola za m’minda.+Anapitirizanso kumudyetsa uchi wochokera m’thanthwe,+Ndi mafuta ochokera m’mwala wa nsangalabwi.+ Deuteronomo 33:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Kwa Aseri anati:+“Aseri ndi wodalitsidwa ndi ana aamuna.+Akhale wovomerezeka ndi abale ake,+Woponda phazi lake m’mafuta.+
24 Kwa Aseri anati:+“Aseri ndi wodalitsidwa ndi ana aamuna.+Akhale wovomerezeka ndi abale ake,+Woponda phazi lake m’mafuta.+