Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Iye ndi Thanthwe, ndipo ntchito yake ndi yangwiro,+

      Njira zake zonse ndi zolungama.+

      Mulungu wokhulupirika,+ amene sachita chosalungama.+

      Iye ndi wolungama ndi wowongoka.+

  • Deuteronomo 32:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Anapitiriza kumuyendetsa pamapiri a dziko lapansi,+

      Moti anadya zokolola za m’minda.+

      Anapitirizanso kumudyetsa uchi wochokera m’thanthwe,+

      Ndi mafuta ochokera m’mwala wa nsangalabwi.+

  • Deuteronomo 33:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kwa Aseri anati:+

      “Aseri ndi wodalitsidwa ndi ana aamuna.+

      Akhale wovomerezeka ndi abale ake,+

      Woponda phazi lake m’mafuta.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena