Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 9:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Inu ndinu wolungama+ pa zinthu zonse zimene zatichitikira, pakuti inu mwachita zinthu mokhulupirika+ koma ife tachita zinthu zoipa.+

  • Salimo 20:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Tidzafuula mokondwera chifukwa cha chipulumutso chanu,+

      Tidzakweza mbendera zathu m’dzina la Mulungu wathu.+

      Yehova akwaniritse zopempha zanu zonse.+

  • Salimo 35:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Lilime langa linene chapansipansi za chilungamo chanu,+

      Ndipo likutamandeni tsiku lonse.+

  • Salimo 59:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma ine, ndidzaimba za mphamvu yanu,+

      M’mawa ndidzanena mosangalala za kukoma mtima kwanu kosatha.+

      Pakuti inu mwakhala malo anga okwezeka ndiponso achitetezo,+

      Ndiponso malo anga othawirako pa nthawi ya masautso.+

  • Danieli 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Inu Yehova ndinu wolungama, koma ife manyazi aphimba nkhope zathu lero.+ Manyazi aphimba nkhope za amuna a mu Yuda, anthu a ku Yerusalemu ndi anthu onse a ku Isiraeli, amene ali pafupi ndiponso amene ali kumayiko onse akutali kumene munawabalalitsira chifukwa cha zinthu zosakhulupirika zimene anakuchitirani.+

  • Aroma 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndipo posadziwa chilungamo cha Mulungu,+ iwo sanagonjere chilungamocho+ koma anayesetsa kukhazikitsa chawochawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena