Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Pa chiyambi,+ Mulungu+ analenga+ kumwamba ndi dziko lapansi.+

  • Genesis 2:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Motero, kumwamba ndi dziko lapansi ndi zonse za mmenemo zinamalizidwa kulengedwa.+

  • Yobu 38:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Kodi unali kuti pamene ndinkaika maziko a dziko lapansi?+

      Ndiuze ngati uli womvetsa zinthu.

  • Yesaya 48:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Komanso dzanja langa linayala maziko a dziko lapansi,+ ndipo dzanja langa lamanja linatambasula kumwamba.+ Ndimafuulira maziko a dziko lapansi ndi kumwamba, kuti ziimirire.+

  • Zekariya 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Uthenga wokhudza Isiraeli:

      “Awa ndi mawu a Yehova okhudza Isiraeli.” Yehova, amene anatambasula miyamba+ ndi kuyala maziko a dziko lapansi+ komanso kupanga mzimu+ n’kuuika mwa munthu, wanena kuti:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena