Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Pa chiyambi,+ Mulungu+ analenga+ kumwamba ndi dziko lapansi.+

  • Nehemiya 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Inu ndinu Yehova, inu nokha.+ Ndinu amene munapanga kumwamba,+ ngakhale kumwambamwamba ndi makamu ake onse.+ Ndinu amene munapanga dziko lapansi+ ndi zonse zili momwemo+ komanso nyanja+ ndi zonse zili momwemo.+ Ndinu amene mukusunga zinthu zonse kuti zikhale ndi moyo. Ndipo makamu+ akumwamba amakugwadirani.

  • Salimo 104:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mwakhazikitsa dziko lapansi pamaziko olimba.+

      Silidzagwedezeka mpaka kalekale, mpaka muyaya.+

  • Salimo 136:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Yamikani woyala dziko lapansi pamwamba pa madzi:+

      Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

  • Miyambo 8:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 pamene anaikira nyanja lamulo lake lakuti madzi ake asapitirire pamene anawalamula,+ pamene anakhazikitsa maziko a dziko lapansi,+

  • Aheberi 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iye akunenanso kuti: “Inu Ambuye, pachiyambipo munaika maziko a dziko lapansi, ndipo kumwamba ndiko ntchito ya manja anu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena