Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tsopano, tamvera. Ndikutuma kwa Farao kuti ukatulutse anthu anga ana a Isiraeli ku Iguputo.”+

  • Ekisodo 4:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho pita. Ine ndidzakhala nawe polankhula ndipo ndidzakuuza zonena.”+

  • Ekisodo 6:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Pita kwa Farao, mfumu ya Iguputo,+ ukamuuze kuti alole ana a Isiraeli kutuluka m’dziko lake.”+

  • Salimo 77:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Mwatsogolera anthu anu ngati nkhosa,+

      Kudzera mwa Mose ndi Aroni.+

  • Machitidwe 7:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ine ndaona ndithu mmene anthu anga amene ali ku Iguputo akuwazunzira.+ Ndamva kubuula kwawo+ ndipo ndatsika kudzawalanditsa.+ Tsopano tamvera. Ndikufuna ndikutume ku Iguputo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena