Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 16:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Choncho zinachitikadi kuti madzulo kunabwera zinziri+ zimene zinakuta msasa wonse, ndipo m’mawa kunachita mame kuzungulira msasa wonsewo.+

  • Numeri 11:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Ndiyeno anthuwo anayamba kugwira zinzirizo. Anazigwira masana onse mpaka usiku wonse, mpakanso tsiku lotsatira osalekeza. Amene anagwira zokwana mahomeri* 10+ ndiwo amene anagwira zochepa. Ndipo anali kuziyanika paliponse, moti zinangoti mbwee, pamsasa wonsewo.

  • Salimo 78:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Iye anagwetsa chakudya pa iwo ngati fumbi.+

      Anawagwetsera zolengedwa zamapiko zouluka, zochuluka ngati mchenga wakunyanja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena