Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 104:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndidzaimbira Yehova moyo wanga wonse.+

      Ndidzaimba nyimbo zotamanda Mulungu wanga nthawi yonse ya moyo wanga.+

  • Machitidwe 16:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Koma chapakati pa usiku,+ Paulo ndi Sila anali kupemphera ndi kutamanda Mulungu poimba nyimbo,+ ndipo akaidi ena anali kuwamva.

  • Aefeso 5:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mukakhala pakati panu muziimba masalimo,+ nyimbo zotamanda+ Mulungu, ndiponso nyimbo zauzimu. Muziimba+ nyimbo zotamanda+ Yehova m’mitima mwanu,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena