Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 86:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ikani chizindikiro cha ubwino wanu pa ine,

      Kuti anthu odana nane aone zimenezi ndi kuchita manyazi,+

      Pakuti inu Yehova mwandithandiza ndi kundilimbikitsa.+

  • Salimo 102:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Musandibisire nkhope yanu pa tsiku limene ndili m’masautso aakulu.+

      Tcherani khutu lanu kwa ine.+

      Fulumirani kundiyankha pa tsiku limene ndikuitana.+

  • Yesaya 51:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pakuti Yehova adzatonthoza Ziyoni.+ Iye adzatonthozadi malo ake onse owonongedwa.+ Adzachititsa chipululu chake kukhala ngati Edeni+ ndi dera lake lachipululu kukhala ngati munda wa Yehova.+ Mwa iye mudzakhala kusangalala ndi kukondwera, kuyamikira ndi kuimba nyimbo.+

  • Yesaya 66:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mofanana ndi munthu amene mayi ake amamutonthoza, inenso ndidzakutonthozani anthu inu,+ ndipo mudzatonthozedwa chifukwa cha Yerusalemu.+

  • 2 Akorinto 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Atamandike Mulungu ndi Atate+ wa Ambuye wathu Yesu Khristu, Tate wachifundo chachikulu+ ndi Mulungu amene amatitonthoza m’njira iliyonse,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena