Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 48:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Yehova ndi wamkulu ndi woyenera kutamandidwa kwambiri,+

      Mumzinda wa Mulungu wathu,+ m’phiri lake loyera.+

  • Salimo 96:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Pakuti Yehova ndi wamkulu+ ndi woyenera kutamandidwa kwambiri.

      Iye ndi wochititsa mantha kuposa milungu ina yonse.+

  • Salimo 147:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ambuye wathu ndi wamkulu ndipo ali ndi mphamvu zochuluka.+

      Nzeru zake zilibe malire.+

  • Salimo 150:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mutamandeni chifukwa cha ntchito zake zamphamvu.+

      Mutamandeni mogwirizana ndi ukulu wake wosaneneka.+

  • Aroma 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Chilengedwere dziko kupita m’tsogolo,+ makhalidwe a Mulungu osaoneka+ ndi maso akuonekera bwino. Makhalidwe a Mulungu amenewa, ngakhalenso mphamvu zake zosatha+ ndiponso Umulungu+ wake, zikuonekera m’zinthu zimene anapanga+ moti anthuwo alibenso chifukwa chomveka chosakhulupirira kuti kuli Mulungu.+

  • Chivumbulutso 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iwo akuimba nyimbo ya Mose+ kapolo wa Mulungu, ndi nyimbo ya Mwanawankhosa,+ yakuti:

      “Ntchito zanu n’zazikulu ndi zodabwitsa,+ inu Yehova Mulungu Wamphamvuyonse.+ Njira zanu ndi zolungama ndi zoona,+ inu Mfumu yamuyaya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena